Yakobo 2:9 - Buku Lopatulika9 koma ngati musamala maonekedwe, muchita uchimo, ndipo mutsutsidwa ndi chilamulo monga olakwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 koma ngati musamala maonekedwe, muchita uchimo, ndipo mutsutsidwa ndi chilamulo monga olakwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma mukamaonetsa kukondera, mukuchimwa, ndipo Malamulo a Mulungu akukutsutsani kuti ndinu opalamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma mukamaonetsa tsankho mukuchimwa, ndipo ndinu wochimwa monga wophwanya lamulo. Onani mutuwo |