Yakobo 2:6 - Buku Lopatulika6 Koma inu mumanyoza munthu wosauka. Kodi sakusautsani inu achuma, nakukokerani iwowa kumabwalo a milandu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma inu mumanyoza munthu wosauka. Kodi sakusautsani inu achuma, nakukokerani iwowa kumabwalo a milandu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma inuyo mwakhala mukumnyoza mmphaŵiyo. Kodi si anthu olemera amene amakupsinjani? Si anthu olemera kodi amene amakukokerani ku mabwalo amilandu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma mwakhala mukunyoza amphawi. Kodi si anthu olemerawa amene akukudyerani masuku pamutu? Si anthu amenewa amene amakukokerani ku bwalo la milandu? Onani mutuwo |