Yakobo 1:4 - Buku Lopatulika4 Koma chipiriro chikhale nayo ntchito yake yangwiro, kuti mukakhale angwiro ndi opanda chilema, osasowa kanthu konse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma chipiriro chikhale nayo ntchito yake yangwiro, kuti mukakhale angwiro ndi opanda chilema, osasowa kanthu konse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma kulimbika kumeneku kuzigwira ntchito yake kotheratu, kuti mukhale angwiro, opanda chilema ndi osapereŵera pa kanthu kalikonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Chipiriro chiyenera kugwira ntchito yake kuti mukhale okhwima ndi angwiro, osasowa kanthu kalikonse. Onani mutuwo |