Yakobo 1:14 - Buku Lopatulika14 koma munthu aliyense ayesedwa pamene chilakolako chake cha iye mwini chimkokera, ndikumnyenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma munthu aliyense ayesedwa pamene chilakolako chake cha iye mwini chimkokera, nichimnyenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma munthu aliyense amayesedwa ndi zinyengo pamene chilakolako cha mwiniwakeyo chimkopa ndi kumkola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma munthu aliyense amayesedwa akakokedwa ndi zilakolako zake zoyipa ndi kukopedwa nazo. Onani mutuwo |