Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Tito 2:6 - Buku Lopatulika

6 Momwemonso anyamata uwadandaulire akhale odziletsa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Momwemonso anyamata uwadandaulire akhale odziletsa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Momwemonso amuna achinyamata uŵauzitse kuti akhale odzigwira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Momwemonso, uwalimbikitse amuna achichepere kuti akhale odziletsa.

Onani mutuwo Koperani




Tito 2:6
9 Mawu Ofanana  

anyamata anandiona nabisala, okalamba anandinyamukira, nakhala chilili.


Anyamata ndiponso anamwali; okalamba pamodzi ndi ana.


Kondwera ndi unyamata wako, mnyamata iwe; mtima wako nukasangalale masiku a unyamata wako, nuyende m'njira za mtima wako, ndi monga maso ako aona; koma dziwitsa kuti Mulungu adzanena nawe mlandu wa zonsezi.


Ukumbukirenso Mlengi wako masiku a unyamata wako, asanadze masiku oipa, ngakhale zisanayandikire zakazo zakuti udzati, Sindikondwera nazo;


Ndipo kudzachitika m'tsogolo mwake, ndidzatsanulira mzimu wanga pa anthu onse, ndi ana aamuna ndi aakazi adzanenera, akuluakulu anu adzalota maloto, anyamata anu adzaona masomphenya;


chifukwa chake tsono tisagone monga otsalawo, komatu tidikire, ndipo tisaledzere.


Mkulu usamdzudzule, komatu umdandaulire ngati atate; anyamata ngati abale;


Momwemonso, anyamata inu, mverani akulu. Koma nonsenu muvale kudzichepetsa kuti mutumikirane; pakuti Mulungu akaniza odzikuza, koma apatsa chisomo kwa odzichepetsa.


Ndikulemberani, atate, popeza mwamzindikira Iye amene ali kuyambira pachiyambi. Ndikulemberani, anyamata, popeza mwamgonjetsa woipayo. Ndakulemberani, ana, popeza mwazindikira Atate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa