Tito 2:4 - Buku Lopatulika4 kuti akalangize akazi aang'ono akonde amuna ao, akonde ana ao, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kuti akalangize akazi aang'ono akonde amuna ao, akonde ana ao, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 kuti choncho athe kuphunzitsa azimai achitsikana kukonda amuna ao ndi ana ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono atha kulangiza amayi achichepere kukonda amuna awo ndi ana awo. Onani mutuwo |