Tito 1:3 - Buku Lopatulika3 koma pa nyengo za Iye yekha anaonetsa mau ake muulalikiro, umene anandisungitsa ine, monga mwa lamulo la Mpulumutsi wathu Mulungu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 koma pa nyengo za Iye yekha anaonetsa mau ake muulalikiro, umene anandisungitsa ine, monga mwa lamulo la Mpulumutsi wathu Mulungu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pa nthaŵi yake Mulungu, Mpulumutsi wathu, adaululadi mau ake, ndipo adalamula kuti ine ndipatsidwe udindo wolalika uthengawu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pa nthawi yake Mulungu, Mpulumutsi wathu anawulula poyera mawu ake ndipo analamula kuti ndipatsidwe udindo wolalikira uthengawu. Onani mutuwo |