Rute 4:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo woombolera anati, Sindikhoza kuuombola kwa ine ndekha, ndingaononge cholowa changa; udzitengere wekha mphamvu yanga yakuombola; popeza sinditha kuombola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo woombolera anati, Sindikhoza kuuombola kwa ine ndekha, ndingaononge cholowa changa; udzitengere wekha mphamvu yanga yakuombola; popeza sinditha kuombola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Apo wachibaleyo adati, “Sindingathe kugula mundawo kuti ukhale wanga, kuwopa kuti ndingaononge choloŵa changa. Mugule ndinu, ine sindingathe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamenepo wachibaleyo anati, “Sindingathe kuwuwombola mundawu kuti ukhale wanga, kuopa kuti kutaya cholowa changa. Mugule ndinu. Ine sindingathe.” Onani mutuwo |