Rute 1:5 - Buku Lopatulika5 Koma Maloni ndi Kilioni anamwalira onse awiri; motero ana ake aamuna awiri ndi mwamuna wake anamsiya mkaziyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma Maloni ndi Kilioni anamwalira onse awiri; motero ana ake amuna awiri ndi mwamuna wake anamsiya mkaziyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma Maloni ndi Kiliyoni adamwalira, kotero kuti Naomi adataya ana ake aŵiri aja, pamodzi ndi mwamuna wake yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Maloni ndi Kiliyoni anamwaliranso kotero kuti Naomi anatsala yekha wopanda ana ake awiri aja ndi mwamuna wake. Onani mutuwo |