Numeri 8:2 - Buku Lopatulika2 Nena kwa Aroni, nuti naye, Pamene uyatsa nyalizo, nyali zisanu ndi ziwirizo ziwale pandunji pake pa choikaponyalicho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nena kwa Aroni, nuti naye, Pamene uyatsa nyalizo, nyali zisanu ndi ziwirizo ziwale pandunji pake pa choikapo nyalicho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Uza Aroni kuti, pamene ukuika nyale, uike zisanu ndi ziŵiri, ndipo ziwunikire patsogolo pa choikaponyale.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Yankhula ndi Aaroni kuti pamene uyimika nyale zisanu ndi ziwiri, nyalezo ziziyaka kutsogolo kwa choyikapo nyale.” Onani mutuwo |