Numeri 7:48 - Buku Lopatulika48 Tsiku lachisanu ndi chiwiri kalonga wa ana a Efuremu Elisama mwana wa Amihudi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Tsiku lachisanu ndi chiwiri kalonga wa ana a Efuremu Elisama mwana wa Amihudi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Tsiku lachisanu ndi chiŵiri linali la Elisama mwana wa Amihudi, mtsogoleri wa Aefuremu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri Elisama mwana wa Amihudi, mtsogoleri wa fuko la Efereimu, anabweretsa chopereka chake. Onani mutuwo |