Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 4:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo udikiro wa akatundu ao, monga mwa ntchito zao zonse m'chihema chokomanako ndi ichi: matabwa a Kachisi, ndi mitanda yake, ndi mizati ndi nsanamira zake, ndi makamwa ake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo udikiro wa akatundu ao, monga mwa ntchito zao zonse m'chihema chokomanako ndi ichi: matabwa a Kachisi, ndi mitanda yake, ndi mizati ndi nsanamira zake, ndi makamwa ake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Zimene iwo alamulidwa kuti anyamule pa ntchito yao ya m'chihema chamsonkhano nazi: anyamule mitengo ya malo opatulika monga mafulemu ake, mizati yake ndi masinde ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Ntchito yawo pamene azikatumikira mu tenti ya msonkhano ndi iyi: kunyamula matabwa a chihema, mitanda, mizati ndi matsinde,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:31
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.


Uwawerenge kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuchita ntchito ya chihema chokomanako.


ndi nsichi za kubwalo kozungulira, ndi makamwa ake, ndi zichiri zake, ndi zingwe zake, pamodzi ndi zipangizo zake zonse, ndi ntchito yake yonse; ndipo muziwerenga zipangizo za udikiro wa akatundu ao ndi kuwatchula maina ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa