Numeri 31:2 - Buku Lopatulika2 Abwezereni chilango Amidiyani chifukwa cha ana a Israele; utatero udzaitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Abwezereni chilango Amidiyani chifukwa cha ana a Israele; utatero udzaitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ulipsire Amidiyani chifukwa cha zimene adachitira Aisraele, tsono pambuyo pake udzafa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Uwabwezere zoyipa Amidiyani chifukwa cha zimene anachitira Aisraeli. Ukatha kuchita zimenezi, iwe udzamwalira.” Onani mutuwo |