Numeri 3:46 - Buku Lopatulika46 Kunena za mazana awiri ndi makumi asanu ndi awiri kudza atatuwo oyamba kubadwa a ana a Israele, akuposa Alevi, akaomboledwe, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Kunena za mazana awiri ndi makumi asanu ndi awiri kudza atatuwo oyamba kubadwa a ana a Israele, akuposa Alevi, akaomboledwe, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Pofuna kuwombola ana achisamba 273 a Aisraele amene aposa chiŵerengero cha amuna a fuko la Levi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Pofuna kuwombola ana aamuna 273 oyamba kubadwa a Aisraeli amene anaposa chiwerengero cha aamuna a fuko la Levi, Onani mutuwo |