Numeri 27:19 - Buku Lopatulika19 numuimike pamaso pa Eleazara wansembe, ndi pamaso pa khamu lonse; numlangize pamaso pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 numuimike pamaso pa Eleazara wansembe, ndi pamaso pa khamu lonse; numlangize pamaso pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Umuimiritse pamaso pa wansembe Eleazara ndi pamaso pa mpingo wonse, tsono umlonge m'malo mwako, iwo akupenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Umuyimiritse pamaso pa wansembe Eliezara ndi pamaso pa gulu lonse ndipo umupatse mphamvu zolamulira, anthuwo akuona. Onani mutuwo |