Numeri 27:17 - Buku Lopatulika17 wakutuluka pamaso pao, ndi kulowa pamaso pao, wakuwatulutsa ndi kuwalowetsa; kuti khamu la Yehova lisakhale ngati nkhosa zopanda mbusa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 wakutuluka pamaso pao, ndi kulowa pamaso pao, wakuwatulutsa ndi kuwalowetsa; kuti khamu la Ambuye lisakhale ngati nkhosa zopanda mbusa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Munthuyo aziŵatsogolera pa nkhondo ndi kuŵalamula, kuti mpingo wanu usamakhale ngati nkhosa zopanda mbusa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 alitsogolere potuluka ndi polowa, kuti anthu a Yehova asakhale ngati nkhosa zopanda mʼbusa.” Onani mutuwo |