Numeri 26:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo mwana wamwamuna wa Sutela ndiye Erani, ndiye kholo la banja la Aerani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo mwana wamwamuna wa Sutela ndiye Erani, ndiye kholo la banja la Aerani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Ndipo ana aamuna a Sutela anali aŵa: Erani anali kholo la banja la Aerani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Zidzukulu za Sutela zinali izi: kuchokera mwa Erani, fuko la Aerani. Onani mutuwo |