Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo mwana wamwamuna wa Sutela ndiye Erani, ndiye kholo la banja la Aerani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo mwana wamwamuna wa Sutela ndiye Erani, ndiye kholo la banja la Aerani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Ndipo ana aamuna a Sutela anali aŵa: Erani anali kholo la banja la Aerani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Zidzukulu za Sutela zinali izi: kuchokera mwa Erani, fuko la Aerani.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:36
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Efuremu: Sutela, ndi Beredi mwana wake, ndi Tahati mwana wake, ndi Eleada mwana wake, ndi Tahati mwana wake,


Ana aamuna a Efuremu monga mwa mabanja ao ndiwo: Sutela, ndiye kholo la banja la Asutela; Bekere, ndiye kholo la banja la Abekere; Tahani, ndiye kholo la banja la Atahani.


Iwo ndiwo mabanja a ana a Efuremu monga mwa owerengedwa ao, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana asanu. Iwo ndiwo ana aamuna a Yosefe monga mwa mabanja ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa