Numeri 21:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo Israele analanda mizinda iyi yonse; nakhala Israele m'mizinda yonse ya Aamori; mu Hesiboni ndi midzi yake yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo Israele analanda midzi iyi yonse; nakhala Israele m'midzi yonse ya Aamori; m'Hesiboni ndi milaga yake yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Aisraele adalanda mizinda yonseyi nakhala m'mizinda yonse ya Aamori, ku Hesiboni ndi m'midzi yake yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ndipo Aisraeli analanda mizinda yonse ya Aamori, nakhalamo kuphatikizapo Hesiboni ndi midzi yake yozungulira. Onani mutuwo |