Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:33 - Buku Lopatulika

33 Koma sanawerenge Alevi mwa ana a Israele; monga Yehova adauza Mose.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Koma sanawerenge Alevi mwa ana a Israele; monga Yehova adauza Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Koma Alevi sadaŵaŵerengere kumodzi ndi Aisraele, monga momwe Chauta adaalamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Koma Alevi sanawawerenge pamodzi ndi Aisraeli enawo monga momwe Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:33
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose, momwemo anamanga mahema ao pa mbendera zao, momwemonso anayenda paulendo, yense monga mwa mabanja ake, monga mwa nyumba za makolo ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa