Numeri 19:11 - Buku Lopatulika11 Iye wakukhudza mtembo wa munthu aliyense adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Iye wakukhudza mtembo wa munthu aliyense adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Amene akhudza mtembo wa munthu wina aliyense, akhala woipitsidwa masiku asanu ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Aliyense wokhudza mtembo wa munthu wina aliyense adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri. Onani mutuwo |