Numeri 18:14 - Buku Lopatulika14 Zilizonse zoperekedwa chiperekere mu Israele ndi zako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Zilizonse zoperekedwa chiperekere m'Israele ndi zako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chinthu chilichonse chimene anthu amapatulira Chauta m'dziko la Israele chikhale chanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Chilichonse mu Israeli chomwe chapatulidwira Yehova ndi chako. Onani mutuwo |