Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:38 - Buku Lopatulika

38 Nena ndi ana a Israele, nuwauze kuti adziombere mphonje m'mphepete mwa zovala zao, mwa mibadwo yao, naike pamphonje m'mphepetemo thonje lamadzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Nena ndi ana a Israele, nuwauze kuti adziombere mphonje m'mphepete mwa zovala zao, mwa mibadwo yao, naike pamphonje m'mphepetemo thonje lamadzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 “Lankhula ndi Aisraele, ndipo uŵauze kuti pa mibadwo yao yonse azisokerera mphonje pa ngodya za zovala, ndipo pa mphonje ya ngodya iliyonse asokerepo chingwe chobiriŵira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 “Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Pa mibado yanu yonse muzisokerera mphonje pa ngodya za zovala zanu ndipo pa ngodya ya mphonje iliyonse azisokererapo chingwe chobiriwira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:38
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Koma amachita ntchito zao zonse kuti aonekere kwa anthu; pakuti akulitsa chitando chake cha njirisi zao, nakulitsa mphonje,


Ndipo onani, mkazi, anali ndi nthenda yachidwalire zaka khumi ndi ziwiri, anadza pambuyo pake, nakhudza mphonje ya chofunda chake;


anadza pambuyo pake, nakhudza mphonje ya chovala chake; ndipo pomwepo nthenda yake inaleka.


Mudzipangire mphonje pangodya zinai za chofunda chanu chimene mudzifunda nacho.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa