Numeri 14:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Mose anati kwa Yehova, Pamenepo Aejipito adzamva; popeza munakweza anthu awa ndi mphamvu yanu kuwachotsa pakati pao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Mose anati kwa Yehova, Pamenepo Aejipito adzamva; popeza munakweza anthu awa ndi mphamvu yanu kuwachotsa pakati pao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma Mose adayankha Chauta kuti, “Zimenezitu Aejipito adzazimva, pakuti ndinu amene mudaŵatulutsa anthu ameneŵa m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mose anati kwa Yehova, “Aigupto adzamva zimenezi! Mwa mphamvu yanu munawatulutsa anthu amenewa pakati pawo. Onani mutuwo |