Numeri 13:21 - Buku Lopatulika21 Pamenepo anakwerako, nazonda dziko kuyambira chipululu za Zini kufikira Rehobu, polowa ku Hamati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pamenepo anakwerako, nazonda dziko kuyambira chipululu za Zini kufikira Rehobu, polowa ku Hamati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Choncho adapita kukazonda dzikolo kuyambira ku chipululu cha Zini mpaka ku Rehobu pafupi ndi chipata cha Hamati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Choncho anapita kukazonda dzikolo kuchokera ku chipululu cha Zini mpaka ku Rehobu, mopenyana ndi Lebo Hamati. Onani mutuwo |