Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 13:13 - Buku Lopatulika

13 Wa fuko la Asere, Seturi mwana wa Mikaele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Wa fuko la Asere, Seturi mwana wa Mikaele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 M'fuko la Asere, adatuma Seturi mwana wa Mikaele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 kuchokera ku fuko la Aseri, Seturi mwana wa Mikayeli;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:13
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Wa fuko la Dani, Amiyele mwana wa Gemali.


Wa fuko la Nafutali, Nabi mwana wa Vofusi.


Pamenepo khamu lonse linakweza mau ao, nafuula; ndipo anthuwo analira usikuwo.


Pamenepo tinayenda ulendo kuchokera ku Horebu, ndi kubzola m'chipululu chachikulu ndi choopsa chija chonse munachionachi, panjira ya ku mapiri a Aamori, monga Yehova Mulungu wathu anatiuza; ndipo tinadza ku Kadesi-Baranea.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa