Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:36 - Buku Lopatulika

36 Ndi pakupumula ili anati, Bwerani Yehova kwa zikwizikwi za Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndi pakupumula ili anati, Bwerani Yehova kwa zikwizikwi za Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Mtambowo ukaima, Mose ankati, “Inu Chauta, bwererani kwa Aisraele anu amene ali zikwi zosaŵerengeka.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 “Pamene likupumula, ankanena kuti, “Bwererani, Inu Yehova, ku chinamtindi cha Aisraeli.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:36
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamdalitsa Rebeka, nati kwa iye, Mlongo wathu ndiwe, iwe ukhale amai wa anthu zikwizikwi, mbeu zako zigonjetse chipata cha iwo akudana nao.


Ukani, Yehova, lowani ku mpumulo wanu; Inu ndi hema wa mphamvu yanu.


Yehova bwanji mwatisocheretsa kusiya njira zanu, ndi kuumitsa mitima yathu tisakuopeni? Bwerani, chifukwa cha atumiki anu, mafuko a cholowa chanu.


Yehova Mulungu wanu anakuchulukitsani, ndipo taonani, lero muchuluka ngati nyenyezi za kumwamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa