Numeri 1:37 - Buku Lopatulika37 owerengedwa ao a fuko la Benjamini, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 owerengedwa ao a fuko la Benjamini, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Benjamini, adapezeka kuti ali 35,400. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Benjamini chinali 35,400. Onani mutuwo |