Numeri 1:31 - Buku Lopatulika31 owerengedwa ao a fuko la Zebuloni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 owerengedwa ao a fuko la Zebuloni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Zebuloni, adapezeka kuti ali 57,400. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Zebuloni chinali 57,400. Onani mutuwo |