Numeri 1:29 - Buku Lopatulika29 owerengedwa ao a fuko la Isakara, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 owerengedwa ao a fuko la Isakara, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zinai kudza mazana anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Isakara, adapezeka kuti ali 54,400. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Isakara chinali 54,400. Onani mutuwo |