Numeri 1:27 - Buku Lopatulika27 owerengedwa ao a fuko la Yuda, ndiwo zikwi makumi asanu ndi awiri mphambu zinai kudza mazana asanu ndi limodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 owerengedwa ao a fuko la Yuda, ndiwo zikwi makumi asanu ndi awiri mphambu zinai kudza mazana asanu ndi limodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Yuda, adapezeka kuti ali 74,600. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Yuda chinali 74, 600. Onani mutuwo |