Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:8 - Buku Lopatulika

8 ana a Parosi zikwi ziwiri mphambu zana limodzi kudza makumi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ana a Parosi zikwi ziwiri mphambu zana limodzi kudza makumi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 A banja la Parosi 2,172.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Zidzukulu za Parosi 2,172

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:8
7 Mawu Ofanana  

Ndi Aisraele a ana a Parosi: Ramiya, ndi Iziya, ndi Matikiya, ndi Miyamini, ndi Eleazara, ndi Malikiya, ndi Benaya.


ana a Parosi, zikwi ziwiri ndi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.


Wa ana a Sekaniya, wa ana a Parosi, Zekariya; ndi pamodzi naye, powawerenga monga mwa chibadwidwe chao, amuna zana limodzi mphambu makumi asanu.


Akulu a anthu: Parosi, Pahatimowabu, Elamu, Zatu, Bani,


Rehumu, Hasabuna, Maaseiya,


ndiwo amene anadza ndi Zerubabele: Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu, Baana. Mawerengedwe a amuna a anthu Aisraele ndiwo:


Ana a Sefatiya, mazana atatu mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa