Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:60 - Buku Lopatulika

60 Antchito onse a m'kachisi, ndi ana a akapolo a Solomoni, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

60 Anetini onse, ndi ana a akapolo a Solomoni, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

60 Antchito onse a ku Nyumba ya Mulungu, kuphatikizapo zidzukulu za antchito a Solomoni, onse pamodzi analipo 392.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

60 Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:60
4 Mawu Ofanana  

Okhala m'dziko oyamba tsono, akukhala mwaomwao m'mizinda mwao, ndiwo Israele, ansembe, Alevi, ndi Antchito a m'kachisi.


Antchito onse a m'kachisi, ndi ana a akapolo a Solomoni, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.


ana a Sefatiya, ana a Hatili, ana a Pokereti-Hazebaimu, ana a Amoni.


Ndipo okwera kuchokera ku Telemela, Teleharisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, ndi awa; koma sanakhoze kutchula nyumba za makolo ao, kapena mbumba zao, ngati ali a Israele;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa