Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 3:22 - Buku Lopatulika

22 Ndi potsatizana naye anakonza ansembe okhala kuchidikha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndi potsatizana naye anakonza ansembe okhala kuchidikha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Pambali pa Meremoti, ansembe okhala ku chidikha adakonza chigawo china.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 3:22
4 Mawu Ofanana  

Ana a oimbirawo anasonkhana ochokera ku dziko lozungulira Yerusalemu, ndi kumidzi ya Anetofa,


Potsatizana naye Meremoti mwana wa Uriya mwana wa Hakozi anakonza gawo lina, kuyambira kukhomo la nyumba ya Eliyasibu kufikira malekezero ake a nyumba ya Eliyasibu.


Potsatizana nao anakonza Benjamini ndi Hasubu pandunji pa nyumba pao. Potsatizana nao anakonza Azariya mwana wa Maaseiya mwana wa Ananiya pafupi pa nyumba yake.


anatumiza mau kwa ine Sanibalati ndi Gesemu, kuti, Tiyeni tikomane kumidzi ya ku Chigwa cha Ono; koma analingirira za kundichitira choipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa