Nehemiya 3:22 - Buku Lopatulika22 Ndi potsatizana naye anakonza ansembe okhala kuchidikha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndi potsatizana naye anakonza ansembe okhala kuchidikha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Pambali pa Meremoti, ansembe okhala ku chidikha adakonza chigawo china. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china. Onani mutuwo |