Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 2:2 - Buku Lopatulika

2 Ninena nane mfumu, Nkhope yako nja chisoni chifukwa ninji popeza sudwala? Ichi si chinthu china koma chisoni cha mtima. Pamenepo ndinachita mantha aakulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ninena nane mfumu, Nkhope yako nja chisoni chifukwa ninji popeza sudwala? Ichi si chinthu china koma chisoni cha mtima. Pamenepo ndinachita mantha akulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Apo mfumu idandifunsa kuti, “Kodi bwanji nkhope yako ili yakugwa, pamene sukudwala? Chimenechi si china, koma ndi chisoni chamumtima.” Pamenepo ndidaopa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Tsono mfumu inandifunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani nkhope yako ikuoneka yachisoni pamene iwe sukudwala? Ichi si chinthu china koma chisoni cha mu mtima.” Ine ndinachita mantha kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 2:2
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anafunsa akulu a Farao osungidwa naye m'nyumba ya mbuyake, kuti, Nkhope zanu zagwa bwanji lero?


Chiyembekezo chozengereza chidwalitsa mtima; koma pakufika chifunirocho ndicho mtengo wa moyo.


Mtima wokondwa usekeretsa nkhope; koma moyo umasweka ndi zowawa za m'mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa