Mlaliki 3:18 - Buku Lopatulika18 Ndinati mumtima mwanga, kuti izi zichitika ndi ana a anthu, kuti Mulungu awayese ndi kuti akazindikire eni ake kuti ndiwo nyama zakuthengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndinati mumtima mwanga, kuti izi zichitika ndi ana a anthu, kuti Mulungu awayese ndi kuti akazindikire eni ake kuti ndiwo nyama za kuthengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Kunena za anthu, ndinkalingaliranso kuti, “Mulungu amaŵayesa ndi cholinga choti aŵaonetse kuti iwowo sasiyana konse ndi nyama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndinalingaliranso kuti, “Kunena za anthu, Mulungu amawayesa ndi cholinga choti awaonetse kuti iwo ali ngati nyama. Onani mutuwo |