Mlaliki 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndinati, Kuseka ndi masala; ndi chimwemwe kodi chichita chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndinati, Kuseka ndi masala; ndi chimwemwe kodi chichita chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kukakhala kuseka, ndidati, “Imene ija ndi misala.” Chikakhala chisangalatso, ndidati, “Phindu lake nchiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Kuseka,” ndinati, “imeneyo ndi misala. Ndipo kodi chisangalalo chimabweretsa phindu lanji?” Onani mutuwo |