Mika 3:5 - Buku Lopatulika5 Atero Yehova za aneneri akulakwitsa anthu anga; akuluma ndi mano ao, ndi kufuula, Mtendere; ndipo aliyense wosapereka m'kamwa mwao, amkonzera nkhondo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Atero Yehova za aneneri akulakwitsa anthu anga; akuluma ndi mano ao, ndi kufuula, Mtendere; ndipo aliyense wosapereka m'kamwa mwao, amkonzera nkhondo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Zimene akunena Chauta ndi izi: “Pali aneneri amene amasokeza anthu anga: amamlosera za mtendere amene amaŵadyetsa, koma amamlosera nkhondo amene alibe choŵapatsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova akuti, “Aneneri amene amasocheretsa anthu anga, ngati munthu wina awapatsa chakudya amamufunira ‘mtendere;’ ngati munthu wina sawapatsa zakudya amamulosera zoyipa. Onani mutuwo |