Mika 3:10 - Buku Lopatulika10 Amanga Ziyoni ndi mwazi, ndi Yerusalemu ndi chisalungamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Amanga Ziyoni ndi mwazi, ndi Yerusalemu ndi chisalungamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mumamanga Ziyoni ndi chuma chochipata pakupha anthu, Yerusalemu mumammanga ndi kuipa kwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 inu amene mukumanga Ziyoni pokhetsa magazi, ndi Yerusalemu ndi kuyipa kwanu. Onani mutuwo |