Mateyu 9:21 - Buku Lopatulika21 pakuti analikunena mwa iye yekha, Ngati ndingakhudze chofunda chake chokha ndidzachira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 pakuti analikunena mwa iye yekha, Ngati ndingakhudze chofunda chake chokha ndidzachira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mumtima mwake ankaganiza kuti, “Ndikangokhudza ngakhale chovala chake chokhacho, ndichira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Iyeyo anati mwa iye yekha, “Nditangokhudza kasonga ka mkanjo wake, ine ndidzachiritsidwa.” Onani mutuwo |