Mateyu 3:8 - Buku Lopatulika8 Onetsani inu zipatso zakuyenera kutembenuka mtima: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Onetsani inu zipatso zakuyenera kutembenuka mtima: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chitanitu ntchito zosonyeza kuti mwatembenukadi mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Onetsani chipatso cha kutembenuka mtima. Onani mutuwo |