Mateyu 3:17 - Buku Lopatulika17 ndipo onani, mau akuchokera kumiyamba akuti, Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa, mwa Iyeyu ndikondwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 ndipo onani, mau akuchokera kumiyamba akuti, Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa, mwa Iyeyu ndikondwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono kuthamboko kudamveka mau akuti, “Uyu ndiye Mwana wanga wapamtima. Ndimakondwera naye kwambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye.” Onani mutuwo |