Mateyu 27:41 - Buku Lopatulika41 Chomwechonso ansembe aakulu, pamodzi ndi alembi ndi akulu anamchitira chipongwe, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Chomwechonso ansembe aakulu, pamodzi ndi alembi ndi akulu anamchitira chipongwe, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Nawonso akulu a ansembe pamodzi ndi aphunzitsi a Malamulo ndi akulu a Ayuda ankamuseka. Ankati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Chimodzimodzinso akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anamuchitira chipongwe. Onani mutuwo |