Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 25:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo asanu a iwo anali opusa, ndi asanu anali ochenjera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo asanu a iwo anali opusa, ndi asanu anali ochenjera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Asanu anali opusa, ndipo asanu enawo anali ochenjera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Asanu anali opusa ndipo asanu ena anali ochenjera.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:2
14 Mawu Ofanana  

Dengu limodzi linali ndi nkhuyu zabwinobwino, ngati nkhuyu zoyamba kucha; ndipo dengu limodzi linali ndi nkhuyu zoipaipa, zosadyeka, zinali zoipa.


Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.


Ndani kodi ali kapolo wokhulupirika ndi wanzeru, amene mbuye wake anamkhazika woyang'anira banja lake, kuwapatsa zakudya pa nthawi yake?


Pakuti opusawo, m'mene anatenga nyali zao, sanadzitengerenso mafuta;


koma anzeruwo anatenga mafuta m'nsupa zao, pamodzi ndi nyali zao.


Koma ochenjera anayankha nati, Kapena sangakwanire ife ndi inu; koma makamaka mukani kwa ogulitsa malonda, mukadzigulire inu nokha.


Anatuluka mwa ife, komatu sanali a ife; pakuti akadakhala a ife akadakhalabe ndi ife, koma kudatero kuti aonekere kuti sali onse a ife.


Koma ndifuna kukukumbutsani mungakhale munadziwa zonse kale, kuti Ambuye, atapulumutsa mtundu wa anthu ndi kuwatulutsa m'dziko la Ejipito, anaononganso iwo osakhulupirira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa