Mateyu 24:23 - Buku Lopatulika23 Pomwepo munthu akanena kwa inu, Onani, Khristu ali kuno, kapena uko musamvomereze; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Pomwepo munthu akanena kwa inu, Onani, Khristu ali kuno, kapena uko musamvomereze; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 “Pa nthaŵi imeneyo wina akadzakuuzani kuti, ‘Ali panotu Khristu uja! Uyo ali apoyo!’ musadzakhulupirire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Pa nthawi imeneyo ngati wina adzati kwa inu, ‘Onani, Khristu ali pano!’ Kapena, ‘Uyo ali ukoyo!’ Musakhulupirire. Onani mutuwo |