Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 23:30 - Buku Lopatulika

30 ndi kuti, Ife tikadakhala m'masiku a makolo anthu, sitikadakhala oyanjana nao pa mwazi wa aneneri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 ndi kuti, Ife tikadakhala m'masiku a makolo anthu, sitikadakhala oyanjana nao pa mwazi wa aneneri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Ndiye mumati, ‘Tikadakhala ndi moyo pa nthaŵi ya makolo athu ija, sibwenzi ife titaŵapha nao aneneriwo ai.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ndipo mumati, ‘Ngati tikanakhala mʼmasiku a makolo athu sitikanakhetsa nawo magazi a aneneri.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:30
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova Mulungu wa makolo ao anatumiza kwa iwo ndi dzanja la mithenga yake, nalawirira mamawa kuituma, chifukwa anamvera chifundo anthu ake, ndi pokhala pake;


Ndapanda ana anu mwachabe; sanamvere kulanga; lupanga lanu ladya aneneri anu, monga mkango wakuononga.


Tsoka inu, alembi ndi Afarisi, onyenga! Chifukwa mumanga nyumba za pa manda a aneneri, ndipo mukonza manda a anthu olungama,


Pomwepo mutsimikiza nokha, kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.


Tapenyani Israele monga mwa thupi; kodi iwo akudya nsembezo alibe chiyanjano ndi guwa la nsembe?


Ndipo chiyembekezo chathu cha kwa inu nchokhazikika; podziwa kuti monga muli oyanjana ndi masautsowo, koteronso ndi chitonthozo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa