Mateyu 23:30 - Buku Lopatulika30 ndi kuti, Ife tikadakhala m'masiku a makolo anthu, sitikadakhala oyanjana nao pa mwazi wa aneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 ndi kuti, Ife tikadakhala m'masiku a makolo anthu, sitikadakhala oyanjana nao pa mwazi wa aneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ndiye mumati, ‘Tikadakhala ndi moyo pa nthaŵi ya makolo athu ija, sibwenzi ife titaŵapha nao aneneriwo ai.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ndipo mumati, ‘Ngati tikanakhala mʼmasiku a makolo athu sitikanakhetsa nawo magazi a aneneri.’ Onani mutuwo |