Mateyu 20:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo m'mene khumiwo anamva, anapsa mtima ndi abale awiriwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo m'mene khumiwo anamva, anapsa mtima ndi abale awiriwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Pamene khumi ena aja adamva zimenezi, adapsera mtima abale aŵiri aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ophunzira khumi aja, anawapsera mtima abale awiriwo. Onani mutuwo |