Mateyu 19:22 - Buku Lopatulika22 Koma mnyamatayo m'mene anamva chonenacho, anamuka wachisoni; pakuti anali nacho chuma chambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma mnyamatayo m'mene anamva chonenacho, anamuka wachisoni; pakuti anali nacho chuma chambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma pamene munthu uja adamva mau ameneŵa, adangochokapo ali wovutika mu mtima, chifukwa anali wolemera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mnyamatayo atamva zimenezi, anachoka mokhumudwa, chifukwa anali ndi chuma chambiri. Onani mutuwo |