Mateyu 11:30 - Buku Lopatulika30 Pakuti goli langa lili lofewa, ndi katundu wanga ali wopepuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pakuti goli langa lili lofewa, ndi katundu wanga ali wopepuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Pajatu goli limene ndimakoleka Ine nlosavuta, ndipo katundu amene ndimasenzetsa Ine ngwopepuka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Pakuti goli langa ndi losavuta ndipo katundu wanga ndi wopepuka.” Onani mutuwo |