Mateyu 11:28 - Buku Lopatulika28 Idzani kuno kwa Ine nonsenu akulema ndi kuthodwa, ndipo Ine ndidzakupumulitsani inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Idzani kuno kwa Ine nonsenu akulema ndi kuthodwa, ndipo Ine ndidzakupumulitsani inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 “Bwerani kwa Ine, inu nonse otopa ndi olemedwa, ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 “Idzani kwa Ine, inu nonse otopa ndi olemedwa ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo. Onani mutuwo |