Mateyu 10:36 - Buku Lopatulika36 ndipo apabanja ake a munthu adzakhala adani ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 ndipo apabanja ake a munthu adzakhala adani ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 mwakuti adani a munthu adzakhala a m'banja mwake omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 adani a munthu adzakhala a mʼbanja mwake momwe.’ Onani mutuwo |